Luka 20:46 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cenjerani nao alembi, amene afuna kuyendayenda obvala miinjiro, nakonda kulankhulidwa m'misika, ndi mipando yaulemu m'sunagoge, ndi malo aulemu pamapwando;

Luka 20

Luka 20:44-47