Luka 2:34 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Simeoni anawadalitsa, nati kwa Mariya amace, Taona, Uyu waikidwa akhale kugwa ndi kunyamuka kwa anthu ambiri mwa. Israyeli; ndipo akhale cizindikilo cakutsutsana naco;

Luka 2

Luka 2:28-39