Luka 18:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mfarisiyo anaimirira napemphera izi mwa yekha, Mulungu, ndikuyamikani kuti sindiri monga anthu onse ena, opambapamba, osalungama, acigololo, kapenanso monga wamsonkho uyu;

Luka 18

Luka 18:8-19