Luka 13:28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kudzakhala komweko kulira ndi kukukuta mano, pamene mudzaona Abrahamu, ndi Isake, ndi Yakobo, ndi aneneri onse, mu. Ufumu wa Mulungu, koma inu nokha muturutsidwa kunja.

Luka 13

Luka 13:25-30