59. Ndipo panali 10 tsiku lacisanu ndi citatu iwo anadza kudzadula kamwanako; ndipo akati amuche dzina la atate wace Zakariya.
60. Ndipo amace anayankha, kuti, lai; koma 11 adzachedwa Yohane.
61. Ndipo iwo anati kwa iye, Palibe wina wa abale ako amene achedwa dzina ili.