Luka 1:59-61 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

59. Ndipo panali 10 tsiku lacisanu ndi citatu iwo anadza kudzadula kamwanako; ndipo akati amuche dzina la atate wace Zakariya.

60. Ndipo amace anayankha, kuti, lai; koma 11 adzachedwa Yohane.

61. Ndipo iwo anati kwa iye, Palibe wina wa abale ako amene achedwa dzina ili.

Luka 1