Luka 1:50-54 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

50. 5 Ndipo cifundo cace cifikira anthu a mibadwo mibadwoPa iwo amene amuopa iye.

51. Iye anacita zamphamvu ndi mkono wace;6 Iye anabalalitsa odzitama ndi mlingaliro wa mtima wao,

52. iye anatsitsa mafumu pa mipando yao yacifumu,Ndipo anakweza aumphawi,

53. 7 Anawakhutitsa anjala ndi zinthu zabwino,Ndipo eni cuma anawacotsa opanda kanthu.

54. Anathangatira Israyeli mnyamata wace,Kuti akakumbukile cifundo,

Luka 1