Luka 1:45-50 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

45. Ndipo wodala ali iye amene anakhulupirira; cifukwa zidzacitidwa zinthu zimene Ambuye analankhula naye.

46. 3 Ndipo Mariya anati,Moyo wanga ulemekeza Ambuye,

47. Ndipo mzimu wanga wakondwera mwa Mulungu Mpulumutsi wanga.

48. Cifukwa iye anayang'anira umphawi wa mdzakazi wace;Pakuti taonani, kuyambira tsopano, anthu a mibadwo yonse adzandichula ine wodala.

49. Cifukwa iye Wamphamvuyo anandicitira ine zazikuru;4 Ndipo dzina lace liri loyera.

50. 5 Ndipo cifundo cace cifikira anthu a mibadwo mibadwoPa iwo amene amuopa iye.

Luka 1