Levitiko 8:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anambveka ndi maraya a m'kati, nammanga m'cuuno ndi mpango, nambveka ndi mwinjiro, nambveka ndi efodi, nammanga m'cuuno ndi mpango wa efodi nammanga nao pathupi pace.

Levitiko 8

Levitiko 8:1-16