Levitiko 8:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anaipha; ndi Mose anatenga mwaziwo, naupaka ndi cala cace pa nyanga za guwa la nsembe pozungulira; nayeretsa guwa la nsembe, nathira mwazi patsinde pa guwa la nsembe, nalipatula, kuti alicitire colitetezera.

Levitiko 8

Levitiko 8:6-16