Levitiko 6:28-30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

28. Ndipo mphika wadothi umene anaphikamo nyamayi auswe, koma ngati anaiphika mu mphika wamkuwa, atsuke uwu, nautsukuluze ndi madzi.

29. Amuna onse a mwa ansembe adyeko; ndiyo yopatulikitsa.

30. Koma asadye nsembe yaucimo iri yonse, imene amadza nao mwazi wace ku cihema cokomanako kutetezera nao m'malo opatulika; aitenthe ndi moto.

Levitiko 6