Levitiko 4:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo wansembeyo abviike cala cace m'mwazimo, nawaze mwaziwo kasanu ndi kawiri pamaso pa Yehova cakuno ca nsaru yocinga, ya malo opatulika.

Levitiko 4

Levitiko 4:1-8