Levitiko 27:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Munthu akapatulirako Yehova munda wace wace, uziuyesa monga mwa mbeu zace zikakhala; homeri wa barie uuyese wa masekeli makumi asanu a siliva.

Levitiko 27

Levitiko 27:14-22