Levitiko 25:50 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo awerengere amene anamgulayo kuyambira caka adadzigulitsa kwa iye kufikira caka coliza lipenga; ndipo mtengo wace ukhale monga mwa kuwerenga kwa zaka; amuyesere monga masiku a munthu wolipidwa.

Levitiko 25

Levitiko 25:44-55