11. ndipo mwana wamwamuna wa mkazi M-israyeli anacitira DZINA mwano, natemberera; ndipo anadza naye kwa Mose. Dzina la mai wace ndiye Selomiti, mwana wa Dibri, wa pfuko la Dani.
12. Ndipo anamsunga m'kaidi, kuti awafotokozere m'mene anenere Yehova.
13. Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,