Levitiko 23:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nena ndi ana a Israyeli, ndi kuti, Mwezi wacisanu ndi ciwiri, tsiku loyamba la mweziwo, muzipumula, ndiko cikumbutso ca kuliza malipenga, msonkhano wopatulika.

Levitiko 23

Levitiko 23:17-33