Levitiko 23:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nena ndi ana a Israyeli, nuti nao, Mutakalowa m'dziko limene ndikupatsani, ndi kuceka dzinthu zace, pamenepo muzidza nao mtolo wa zipatso zoyamba za masika anu kwa wansembe;

Levitiko 23

Levitiko 23:3-18