Levitiko 22:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma wansembe atakagula munthu ndi ndarama zace, iyeyu adyeko; ndi iwo amene anabadwa m'nyumba yace, adyeko mkate wace.

Levitiko 22

Levitiko 22:3-20