Levitiko 21:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iye wokhala mkulu wansembe mwa abale ace, amene anamtsanulira mafuta odzoza pamutu pace, amene anamdzaza dzanja kuti abvale zobvalazo, asawinde, kapena kung'amba zobvala zace.

Levitiko 21

Levitiko 21:6-15