Levitiko 21:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova ananena ndi Mose, Nena ndi ansembe, ana a Aroniwo, nuti nao, Asadzidetse mmodzi wa inu cifukwa ca wakufa mwa anthu a mtundu wace;

Levitiko 21

Levitiko 21:1-9