Levitiko 20:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Munthu akagona ndi mkazi ali mumsambo, nakambvula, anabvula kasupe wace, ndi iye mwini anabvula kasupe wa nthenda yace; awadule onse awiri pakati pa anthu a mtundu wao.

Levitiko 20

Levitiko 20:11-21