Levitiko 2:14-16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

14. Ndipo ukabwera nayo nsembe yaufa ya zipatso zoyamba kwa Yehova, uzibwera nayo nsembe yako ya zipatso zoyamba ikhale ya ngala zoyamba kuca, zoumika pamoto, zokonola.

15. Ndipo uthirepo mafuta, ndi kuikapo libona; ndiyo nsembe yaufa.

16. Ndipo wansembe atenthe cikumbutso cace, atatapa pa tirigu wace wokonola, ndi pa mafuta ace, ndi kutenga libano lace lonse; ndiyo nsembe yamoto ya kwa Yehova.

Levitiko 2