12. Usamabvula mlongo wa atate wako; ndiye wa cibale ca atate wako.
13. Usamabvula mbale wa mai wako; popeza ndiye mbale wa mai wako.
14. Usamabvula mbale wa atate wako; usamasendera kwa mkazi wace; ndiye mai wako.
15. Usamabvula mpongozi wako; ndiye mkazi wa mwana wamwamuna wako; usamambvula.