Levitiko 18:12-15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

12. Usamabvula mlongo wa atate wako; ndiye wa cibale ca atate wako.

13. Usamabvula mbale wa mai wako; popeza ndiye mbale wa mai wako.

14. Usamabvula mbale wa atate wako; usamasendera kwa mkazi wace; ndiye mai wako.

15. Usamabvula mpongozi wako; ndiye mkazi wa mwana wamwamuna wako; usamambvula.

Levitiko 18