Levitiko 16:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo atengeko mwazi wa ng'ombeyo, ndi kuuwaza ndi cala cace pacotetezerapo, mbali ya kum'mawa; nawaze mwazi ndi cala cace cakuno ca cotetezerapo kasanu ndi kawiri.

Levitiko 16

Levitiko 16:10-17