Levitiko 15:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ngati mwamuna ali yense agona naye, ndi kudetsa kwace kukhala pa iye, adzakhala wodetsedwa masiku asanu ndi awiri; ndipo kama ali yense agonapo ali wodetsedwa.

Levitiko 15

Levitiko 15:16-33