Levitiko 14:36 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo wansembe aziuza kuti aturutse zonse za m'nyumba, asanalowe kudzaona nthendayi, zinthu zonse ziri m'nyumba zingakhale zodetsedwa; ndipo atatero wansembe alowe kukaona nyumbayi;

Levitiko 14

Levitiko 14:31-46