Levitiko 14:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo wansembe atenge mwana wa nkhosa mmodzi wamwamuna, nabwere naye akhale nsembe yoparamula, pamodzi ndi muyeso uja wa mafuta, naziweyule nsembe yoweyula pamaso pa Yehova.

Levitiko 14

Levitiko 14:8-13