Levitiko 13:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma ngati cikanga cikhala cotuwa pa khungu la thupi lace, ndipo cikaoneka cosapitirira khungu, ndi tsitsi lace losasanduka loyera, pamenepo wansembe ambindikiritse wanthendayo masiku asanu ndi awiri;

Levitiko 13

Levitiko 13:1-14