Levitiko 12:7-8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

7. ndipo iye abwere nayo pamaso pa Yehova, namcitire comtetezera mkaziyo, ndipo adzakhala woyeretsedwa wocira kukha mwazi kwace.

8. Ici ndi cilamulo ca kwa iye wakubala, kapena mwana wamwamuna kapena wamkazi. Ndipo cuma cace cikapanda kufikira nkhosa, atenge njiwa ziwiri kapena maunda awiri; lina likhale nsembe yopsereza, ndi lina nsembe yaucimo; ndi wansembe amcitire comtetezera, ndipo adzakhalawoyera.

Levitiko 12