Levitiko 11:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma muyenera kudya izi mwa zokwawa zonse zakuuluka, zokhala ndi miyendo inai, zokhala ndi miyendo pa mapazi ao, ya kuthumpha nayo pansi; mwa zimenezi muyenera kudya izi:

Levitiko 11

Levitiko 11:20-31