15. kungubwi mwa mtundu wace;
16. ndi nthiwatiwa, ndi cipudo, ndi kakoa, ndi kabawi mwa mtundu wace;
17. ndi nkhutunkhutu ndi nswankhono ndi mancici;
18. tsekwe, bvuwo, ndi dembu;
19. indwa, ndi cimeza monga mwa mtundu wace, ndi sadzu, ndi mleme.
20. Zokwawa zonse zakuuluka zokhala ndi miyendo inai, muziyesa izi zonyansa,