Hoseya 4:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Anthu anga aonongeka cifukwa ca kusadziwa; popeza unakana kudziwa, Inenso ndikukaniza, kuti usakhale wansembe wanga; popeza waiwala cilamulo ca Mulungu wako, Inenso ndidzaiwala ana ako.

Hoseya 4

Hoseya 4:5-9