Hoseya 4:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Anthu anga afunsira ku mtengo wao, ndi ndodo yao iwafotokozera; pakuti mzimu wacigololo wawalakwitsa, ndipo acita cigololo kucokera Mulungu wao.

Hoseya 4

Hoseya 4:2-16