Hoseya 3:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

atatero ana a Israyeli adzabwera, nadzafuna Yehova Mulungu wao, ndi Davide mfumu yao, nadzafika ndi mantha kwa Yehova, ndi ku ukoma wace masiku otsiriza.

Hoseya 3

Hoseya 3:1-5