Hoseya 2:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo adzatsata omkonda koma osawakumika, adzawafunafuna koma osawapeza; pamenepo adzati, Ndidzamuka ndi kubwererana ndi mwamuna wanga woyamba, popeza pamenepo panandikomera koposa tsopano.

Hoseya 2

Hoseya 2:3-10