Hoseya 1:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ciyambi ca kunena kwa Yehova mwa Hoseya, Ndipo Yehova anati kwa Hoseya, Muka, udzitengere mkazi wacigololo ndi ana acigololo; pakuti dziko latsata cigololo cokha cokha kuleka kutsata Yehova.

Hoseya 1

Hoseya 1:1-3