Hagai 2:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Musamalire, kuyambira lero ndi m'tsogolo, kuyambira tsiku la makumi awiri ndi cinai la mwezi wacisanu ndi cinai, kuyambira tsiku lija anamanga maziko a Kacisi wa Yehova, samalirani.

Hagai 2

Hagai 2:9-23