Hagai 1:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndinaitana cirala cidzere dziko, ndi mapiri, ndi tirigu, ndi vinyo, ndi mafuta, ndi zimene ibala nthaka, ndi anthu, ndi zoweta, ndi nchito zonse za manja.

Hagai 1

Hagai 1:1-15