Habakuku 2:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Popeza iwe wafunkha amitundu ambiri, otsala onse a mitundu ya anthu adzakufunkha iwe; cifukwa ca mwazi wa anthu, ndi ciwawa cocitikira dziko, mudzi, ndi onse okhalamo.

Habakuku 2

Habakuku 2:4-14