Habakuku 2:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Udzazidwa nao manyazi m'malo mwa ulemerero; imwa iwenso, nukhale wosadulidwa; cikho ca dzanja lamanja la Yehova cidzatembenukira iwe, ndi kusanza kwa manyazi kudzakhala pa ulemerero wako,

Habakuku 2

Habakuku 2:12-20