Genesis 6:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anati Yehova, Ndidzafafaniza anthu amene ndawalenga pa dziko lapansi; anthu, ndi nyama, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga: pakuti ndimva cisoni cifukwa ndapanga izo.

Genesis 6

Genesis 6:1-9