Genesis 48:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anadalitsa iwo tsiku lomwelo, nati, Mwa iwe Israyeli adzadalitsa, kuti, Mulungu akuyese iwe monga Efraimu ndi monga Manase; ndipo anaika Efraimu woyamba wa Manase.

Genesis 48

Genesis 48:16-22