Genesis 44:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Taonani, ndalama zija, tinazipeza kukamwa kwa matumba athu, tinazibwezanso kwa inu kuturuka m'dziko la Kanani; nanga bwanji tingabe m'nyumba ya mbuyanga kapena siliva kapena golidi?

Genesis 44

Genesis 44:2-17