Genesis 44:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iye anati, Ngati kutheka kuti ndicite cotero! Munthu amene anampeza naco m'dzanja lace adzakhala kapolo wanga: koma inu, kazipitani ndi mtendere kwa atate wanu.

Genesis 44

Genesis 44:7-20