Genesis 42:37 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Rubeni anati kwa atate wace, kuti, Muwaphe ana anga amuna awiri ndikapanda kumbweza iye kwa inu; mumpereke iye m'manja mwanga, ndipo ine ndidzambwezanso kwa inu.

Genesis 42

Genesis 42:27-38