Genesis 36:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Esau anatenga akazi ace a ana akazi a m'Kanani: Ada mwana wamkazi wa Eloni Mhiti, ndi Oholibama mwana wamkazi wa Ana, mwana wamkazi wa Zibeoni Mhivi;

Genesis 36

Genesis 36:1-10