Genesis 31:33 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Labani analowa m'hema wa Yakobo, ndi m'hema wa Leya, ndi m'mahema a adzakazi awiri aja; koma sanapeze, Ndipo anaturuka m'hema wa Leya nalowa m'hema wa Rakele.

Genesis 31

Genesis 31:32-36