Genesis 30:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yakobo anadza madzulo kucokera kumunda, ndipo Leya ananka kukomana naye, nati, Ulowe kwa ine cifukwa ndakulipilira iwe ndi mankhwala a mwana wanga. Ndipo anagona naye usiku womwewo.

Genesis 30

Genesis 30:9-18