Genesis 3:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kwa mkaziyo ndipo anati, Ndidzacurukitsa kusauka kwako ndi potenga mimba pako; udzasauka pakubala: udzakhumba mwamuna wako, ndipo iye adzakulamulira iwe.

Genesis 3

Genesis 3:11-21