Genesis 26:21-23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

21. Ndipo anakumbanso citsime cina, ndipo anakangana naconso; nacha dzina lace Sitina.

22. Ndipo anacoka kumeneko nakumba citsime cina; koma sanakangana naco cimeneco; ndipo anacha dzina lace Rehoboti; ndipo anati, Cifukwa kuti tsopano Yehova anatipatsa ife malo, ndipo tidzabalana m'dziko muno.

23. Ndipo anacoka kumeneko nakwera kunka ku Beereseba,

Genesis 26