Genesis 25:3-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Ndipo Yokesani anabala Seba, ndi Dedani. Ana a Dedani ndi Aasuri, ndi Aletusi, ndi Aleumi.

4. Ana a Midyani: Efa, ndi Efere, ndi Hanoki, ndi Abida, ndi Elida. Onse amenewa ndi ana a Ketura.

5. Ndipo Abrahamu amwali anampatsa Isake zonse anali nazo.

Genesis 25